Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Marko 8:10 - Buku Lopatulika

Ndipo pomwepo analowa m'ngalawa ndi ophunzira ake, nafika ku mbali ya ku Dalamanuta.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo pomwepo analowa m'ngalawa ndi ophunzira ake, nafika ku mbali ya ku Dalamanuta.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pambuyo pake Yesu adatsazikana nawo anthu aja, kenaka Iye ndi ophunzira ake adaloŵa m'chombo napita ku dera la Dalamanuta.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

analowa mʼbwato pamodzi ndi ophunzira ake napita ku dera la Dalamanuta.

Onani mutuwo



Marko 8:10
2 Mawu Ofanana  

Ndipo m'mene Iye anauza makamuwo amuke, analowa m'ngalawa, nafika m'malire a Magadani.


Ndipo iwo anali ngati zikwi zinai; ndipo Iye analawirana nao.