Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Marko 7:12 - Buku Lopatulika

simulolanso kumchitira kanthu atate wake kapena amai wake;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

simulolanso kumchitira kanthu atate wake kapena amai wake;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

ameneyo sasoŵanso kuŵathandiza atate ake ndi amai ake.’

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

pamenepo inu simumalola kuti achitire kanthu kalikonse abambo kapena amayi ake.

Onani mutuwo



Marko 7:12
2 Mawu Ofanana  

koma inu munena, Munthu akati kwa atate wake, kapena amai wake, Korban, ndiko kuti Mtulo, chimene ukadathandizidwa nacho ndi ine,


muyesa achabe mau a Mulungu mwa mwambo wanu, umene munaupereka: ndi zinthu zotere zambiri muzichita.