Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Marko 6:18 - Buku Lopatulika

Pakuti Yohane adanena kwa Herode, Si kuloledwa kwa inu kukhala naye mkazi wa mbale wanu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pakuti Yohane adanena kwa Herode, Si kuloledwa kwa inu kukhala naye mkazi wa mbale wanu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ndipo Yohane adaamuuza kuti, “Nkulakwira Malamulo kulanda mkazi wa mbale wanu.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pakuti Yohane ankanena kwa Herode kuti, “Sikololedwa kwa inu kuti mukwatire mkazi wa mʼbale wanu.”

Onani mutuwo



Marko 6:18
8 Mawu Ofanana  

Koma Mikaya anati, Pali Yehova, zimene Yehova adzanena nane ndidzanena ine.


Usamavula mkazi wa mbale wako; ndiye thupi la mbale wako.


Munthu akatenga mkazi wa mbale wake, chodetsa ichi; wavula mbale wake; adzakhala osaona ana.


Namthira malovu, natenga bango, nampanda Iye pamutu.