Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Marko 6:16 - Buku Lopatulika

Koma Herode pamene anamva, ananena, Yohane amene ndamdula mutu, wauka iyeyo.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Koma Herode pamene anamva, ananena, Yohane amene ndamdula mutu, wauka iyeyo.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pamene Herode adamva zimenezi, adati, “Yohane yemwe ndidamdula pakhosi uja ndiye adauka kwa akufayu.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Koma Herode atamva zimenezi anati, “Yohane, munthu amene ndinamudula mutu, waukitsidwa kuchokera kwa akufa.”

Onani mutuwo



Marko 6:16
8 Mawu Ofanana  

Pamenepo anaopa kwakukulu, popanda chifukwa cha kuopa, pakuti Mulungu anamwaza mafupa a iwo akuzinga iwe; unawachititsa manyazi, pakuti Mulungu anawakaniza.


nanena kwa anyamata ake, Uyo ndiye Yohane Mbatizi; anauka kwa akufa; ndipo chifukwa cha ichi zamphamvuzi zilimbalimba mwa iye.


nanena, Ndinachita koipa ine, pakupereka mwazi wosalakwa. Koma iwo anati, Tili nacho chiyani ife? Udzionere wekha.


Koma ena ananena, kuti, Ndiye Eliya. Anati enanso, Ndiye mneneri, monga ngati mmodzi wa aneneriwo.


Pakuti Herode, mwini yekha, adatuma anthu namgwira Yohane, nammanga m'nyumba yandende, chifukwa cha Herodiasi, mkazi wa Filipo mbale wake; chifukwa adamkwatira iye.


Ndipo Herode anati, Yohane ndinamdula mutu ine; koma uyu ndani ndikumva zotere za iye? Ndipo anafunafuna kumuona Iye.