Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Marko 6:10 - Buku Lopatulika

Ndipo ananena nao, Kumene kulikonse mukalowa m'nyumba, khalani komweko kufikira mukachokako.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo ananena nao, Kumene kulikonse mukalowa m'nyumba, khalani komweko kufikira mukachokako.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Adaŵauzanso kuti, “Mukafika pa mudzi, muzikhala nao kunyumba kumene mudafikirako, mpaka itakwana nthaŵi yoti muchoke kumudziko.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pamene mulowa mʼnyumba mukakhale momwemo kufikira mutachoka mʼmudzimo.

Onani mutuwo



Marko 6:10
7 Mawu Ofanana  

Ndipo pamalo ponse sakulandirani, kapena kumvera inu, pakuchoka kumeneko, sansani fumbi lili kumapazi anu, likhale mboni ya kwa iwo.


koma avale nsapato; ndipo anati, Musavale malaya awiri.


Ndipo m'nyumba iliyonse mukalowemo, khalani komweko, ndipo muzikachokera kumeneko.


Pamene anabatizidwa iye ndi a pabanja pake anatidandaulira ife, kuti, Ngati mwandiyesera ine wokhulupirika kwa Ambuye, mulowe m'nyumba yanga, mugone m'menemo. Ndipo anatiumiriza ife.