Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Marko 6:1 - Buku Lopatulika

Ndipo Iye anatuluka kumeneko; nafika kudziko la kwao; ndipo ophunzira ake anamtsata.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Iye anatuluka kumeneko; nafika kudziko la kwao; ndipo ophunzira ake anamtsata.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Yesu adachoka kumeneko, nakafika kumudzi kwao. Ophunzira ake adatsagana naye.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Yesu anachoka kumeneko napita ku mudzi kwawo, pamodzi ndi ophunzira ake.

Onani mutuwo



Marko 6:1
5 Mawu Ofanana  

Ndipo m'kufesa kwake zina zinagwa m'mbali mwa njira, ndipo zinadza mbalame, nkulusira izo.


nadza nakhazikika m'mzinda dzina lake Nazarete kuti chikachitidwe chonenedwa ndi aneneri kuti, Adzatchedwa Mnazarayo.


Ndipo Yesu ananena kwa iwo, Mneneri sakhala wopanda ulemu, koma m'dziko la kwao ndimo, ndi pakati pa abale ake, ndi m'nyumba yake.