Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Marko 5:8 - Buku Lopatulika

Pakuti ananena kwa iye, Tuluka iwe, mzimu wonyansa, kwa munthuyu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pakuti ananena kwa iye, Tuluka iwe, mzimu wonyansa, kwa munthuyu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Adaatero chifukwa Yesu anali atanena kuti, “Mzimu woipawe, tuluka mwa munthuyu!”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pakuti Yesu anati kwa iye, “Tuluka mwa munthuyu, iwe mzimu woyipa!”

Onani mutuwo



Marko 5:8
5 Mawu Ofanana  

Ndipo Yesu anaudzudzula, kuti, Khala uli chete, nutuluke mwa iye.


ndipo anafuula ndi mau olimba, nanena, Ndili ndi chiyani ine ndi Inu, Yesu Mwana wa Mulungu Wamkulukulu? Ndikulumbirirani pa Mulungu, msandizunze.


Ndipo anamfunsa, Dzina lako ndani? Ndipo ananena kwa Iye, Dzina langa ndine Legio; chifukwa tili ambiri.


Ndipo anachita chotero masiku ambiri. Koma Paulo anavutika mtima ndithu, nacheuka, nati kwa mzimuwo, Ndikulamulira iwe m'dzina la Yesu Khristu, tuluka mwa iye. Ndipo unatuluka nthawi yomweyo.