Marko 5:8 - Buku Lopatulika Pakuti ananena kwa iye, Tuluka iwe, mzimu wonyansa, kwa munthuyu. Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014 Pakuti ananena kwa iye, Tuluka iwe, mzimu wonyansa, kwa munthuyu. Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa Adaatero chifukwa Yesu anali atanena kuti, “Mzimu woipawe, tuluka mwa munthuyu!” Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero Pakuti Yesu anati kwa iye, “Tuluka mwa munthuyu, iwe mzimu woyipa!” |
ndipo anafuula ndi mau olimba, nanena, Ndili ndi chiyani ine ndi Inu, Yesu Mwana wa Mulungu Wamkulukulu? Ndikulumbirirani pa Mulungu, msandizunze.
Ndipo anamfunsa, Dzina lako ndani? Ndipo ananena kwa Iye, Dzina langa ndine Legio; chifukwa tili ambiri.
Ndipo anachita chotero masiku ambiri. Koma Paulo anavutika mtima ndithu, nacheuka, nati kwa mzimuwo, Ndikulamulira iwe m'dzina la Yesu Khristu, tuluka mwa iye. Ndipo unatuluka nthawi yomweyo.