Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Marko 5:10 - Buku Lopatulika

Ndipo anampempha Iye kwambiri kuti asaitulutsire kunja kwake kwa dziko.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo anampempha Iye kwambiri kuti asaitulutsire kunja kwake kwa dziko.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ndipo iye adadandaulira Yesu kwambiri kuti mizimuyo asaitulutsire kunja kwa dera limenelo.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndipo anamupempha Yesu mobwerezabwereza kuti asazitulutse mʼderalo.

Onani mutuwo



Marko 5:10
4 Mawu Ofanana  

Ndipo alembi amene adatsika ku Yerusalemu ananena kuti, Ali naye Belezebulu, ndipo, Ndi mkulu wao wa ziwanda atulutsa ziwanda.


Ndipo panali pamenepo gulu lalikulu la nkhumba zilinkudya kuphiri.


Ndipo anailola. Ndipo mizimu yonyansa inatuluka, nilowa mu nkhumba; ndipo gulu linatsika liwiro potsetsereka ndi kulowa m'nyanja, ndizo ngati zikwi ziwiri; ndipo zinatsamwa m'nyanja.


Ndipo anamfunsa, Dzina lako ndani? Ndipo ananena kwa Iye, Dzina langa ndine Legio; chifukwa tili ambiri.