Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Marko 4:23 - Buku Lopatulika

Ngati munthu ali nao makutu akumva, amve.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ngati munthu ali nao makutu akumva, amve.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Yemwe ali ndi makutu akumva, amve!”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ngati wina ali ndi makutu akumva, amve.”

Onani mutuwo



Marko 4:23
14 Mawu Ofanana  

Amene ali ndi makutu akumva, amve.


Pomwepo olungamawo adzawalitsa monga dzuwa, mu Ufumu wa Atate wao. Amene ali ndi makutu amve.


Amene ali ndi makutu, amve.


Ndipo ananena, Amene ali nao makutu akumva amve.


Suyenera kuuthira pamunda kapena padzala, autaya kunja. Amene ali nao makutu akumva amve.


Ndipo zina zinagwa pa nthaka yokoma, ndipo zinamera, ndi kupatsa zipatso zamakumikhumi. Pakunena Iye izi anafuula, Iye amene ali ndi makutu akumva amve.


Ngati wina ali nalo khutu, amve.


Iye wokhala nalo khutu amve chimene Mzimu anena kwa Mipingo. Iye amene apambana sadzachitidwa choipa ndi imfa yachiwiri.


Iye wakukhala nalo khutu amve chimene Mzimu anena kwa Mipingo. Kwa iye wopambana, ndidzampatsa mana obisika, ndipo ndidzampatsa mwala woyera, ndi pamwalawo dzina latsopano lolembedwapo, wosalidziwa munthu aliyense koma iye wakuulandira.


Iye wokhala nalo khutu amve chimene Mzimu anena kwa Mipingo.


Iye wokhala nalo khutu amve chimene Mzimu anena kwa Mipingo. Kwa iye amene apambana ndidzampatsa kudya za ku mtengo wa moyo umene uli mu Paradaiso wa Mulungu.


Iye wakukhala nalo khutu amve chimene Mzimu anena kwa Mipingo.


Iye wakukhala nalo khutu amve chimene Mzimu anena kwa Mipingo.