Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Marko 4:18 - Buku Lopatulika

Ndipo ena ndiwo akufesedwa kuminga; iwo ndiwo amene adamva mau,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo ena ndiwo akufesedwa kuminga; iwo ndiwo amene adamva mau,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Mbeu zofesedwa pa zitsamba za minga zija zikutanthauza anthu amene amaŵamva mau a Mulungu.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Komabe ena, monga mbewu zofesedwa pakati pa minga, amamva mawu;

Onani mutuwo



Marko 4:18
6 Mawu Ofanana  

Pakuti Yehova atero kwa anthu a Yuda ndi kwa Yerusalemu, Limani masala anu, musabzale paminga.


Ndipo iye amene afesedwa kuminga, uyu ndiye wakumva mau; ndipo kulabadira kwa dziko lapansi, ndi chinyengo cha chuma chitsamwitsa mau, ndipo akhala wopanda chipatso.


ndipo alibe mizu mwa iwo okha, koma akhala kanthawi; pamenepo pakudza masautso kapena mazunzo chifukwa cha mau, pomwepo akhumudwa.


ndipo malabadiro a dziko lapansi, ndi chinyengo cha chuma, ndi kulakalaka kwa zinthu zina, zilowamo, zitsamwitsa mau, ndipo akhala opanda chipatso.


Ndipo zina zinagwa paminga, ndipo minga inakula, nkuzitsamwitsa, ndipo sizinabale zipatso.


Ndipo zija zinagwa kumingazi, ndiwo amene adamva, ndipo m'kupita kwao atsamwitsidwa ndi nkhawa, ndi chuma, ndi zokondweretsa za moyo, ndipo sakhwimitsa zipatso zamphumphu.