Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Marko 3:26 - Buku Lopatulika

Ndipo Satana akadziukira mwini yekha, nagawanika, sangathe kukhazikika, koma atsirizika.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Satana akadziukira mwini yekha, nagawanika, sakhoza kukhazikika, koma atsirizika.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tsono ngati a mu ufumu wa Satana aukirana okhaokha nagaŵikana, Satanayo sangalimbe, ndiye kuti watha basi.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndipo ngati Satana adzitsutsa yekha sangathe kuyima; ulamuliro wake watha.

Onani mutuwo



Marko 3:26
2 Mawu Ofanana  

Pomwepo Yesu ananena kwa iye, Choka Satana, pakuti kwalembedwa, Ambuye Mulungu wako udzamgwadira, ndipo Iye yekhayekha udzamlambira.


Ndipo nyumba ikagawanika pa iyo yokha, singathe kukhazikika nyumbayo.