Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Marko 3:25 - Buku Lopatulika

Ndipo nyumba ikagawanika pa iyo yokha, singathe kukhazikika nyumbayo.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo nyumba ikagawanika pa iyo yokha, sikhoza kukhazikika nyumbayo,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ndipo anthu a m'banja limodzi akayamba kugaŵikana, banja lotere silingalimbe.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ngati nyumba igawanikana mwa iyo yokha, nyumba imeneyo singathe kuyima.

Onani mutuwo



Marko 3:25
7 Mawu Ofanana  

Ndipo abale ake anaona kuti atate wake anamkonda iye koposa abale ake onse: ndipo anamuda iye, ndipo sanathe kulankhula ndi iye mwamtendere.


Onani, nkokoma ndi kokondweretsa ndithu kuti abale akhale pamodzi!


Ndipo ufumu ukagawanika pa uwu wokha, sungathe kukhazikika.


Ndipo Satana akadziukira mwini yekha, nagawanika, sangathe kukhazikika, koma atsirizika.


Koma ngati mulumana ndi kudyana, chenjerani mungaonongane.


Pakuti pomwe pali kaduka ndi zotetana, pamenepo pali chisokonekero ndi chochita choipa chilichonse.