Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Marko 3:19 - Buku Lopatulika

ndi Yudasi Iskariote, ndiye amene anampereka Iye. Ndipo analowa m'nyumba.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

ndi Yudasi Iskariote, ndiye amene anampereka Iye.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

ndiponso Yudasi Iskariote (amene pambuyo pake adapereka Yesu kwa adani ake.)

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

ndi Yudasi Isikarioti, amene anamupereka Iye.

Onani mutuwo



Marko 3:19
13 Mawu Ofanana  

Simoni Mkanani, ndi Yudasi Iskariote amenenso anampereka Iye.


Ndipo Iye ali chilankhulire, onani, Yudasi, mmodzi wa khumi ndi awiriwo, anadza, ndi pamodzi ndi iye khamu lalikulu la anthu, ndi malupanga ndi mikunkhu, kuchokera kwa ansembe aakulu ndi akulu a anthu.


ndi Andrea, ndi Filipo, ndi Bartolomeo, ndi Mateyu, ndi Tomasi, ndi Yakobo mwana wa Alifeyo, ndi Tadeyo, ndi Simoni Mkanani,


Ndipo anthu ambiri anasonkhananso, kotero kuti sanathe iwo konse kudya.


Ndipo iwo anadza ku Kapernao; ndipo pamene anakhala m'nyumba, Iye anawafunsa, Munalikutsutsana ninji panjira?


Ndipo pokhala pamgonero, mdierekezi adatha kuika mu mtima wake wa Yudasi mwana wa Simoni Iskariote, kuti akampereke Iye,


Koma pali ena mwa inu amene sakhulupirira. Pakuti Yesu anadziwa poyamba amene ali osakhulupirira, ndi amene adzampereka.


Koma adanena za Yudasi, mwana wa Simoni Iskariote, pakuti iye ndiye amene akampereka Iye, ali mmodzi wa khumi ndi awiri.