Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Marko 3:13 - Buku Lopatulika

Ndipo anakwera m'phiri, nadziitanira iwo amene anawafuna Iye mwini; ndipo anadza kwa Iye.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo anakwera m'phiri, nadziitanira iwo amene anawafuna Iye mwini; ndipo anadza kwa Iye.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Yesu adakwera ku phiri, ndipo adaitana anthu amene Iye mwini ankaŵafuna, iwo nkupitadi kumene kunali Iyeko.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Yesu anakwera ku phiri ndipo anayitana amene anawafuna, ndipo anabwera kwa Iye.

Onani mutuwo



Marko 3:13
7 Mawu Ofanana  

Ndipo m'mene Iye anaona makamu, anakwera m'phiri; ndipo m'mene Iye anakhala pansi, anadza kwa Iye ophunzira ake;


Ndipo anaika khumi ndi awiri, kuti akhale ndi Iye, ndi kuti akawatume kulalikira,


Ndipo anadziitanira khumi ndi awiriwo, nayamba kuwatumiza iwo awiriawiri; nawapatsa mphamvu pa mizimu yonyansa;


Ndipo Iye anaitana pamodzi khumi ndi awiriwo nawapatsa mphamvu ndi ulamuliro pa ziwanda zonse, ndi zakuchiritsa nthenda.


Koma Yesu anakwera kuphiri, nakhala pansi komweko pamodzi ndi ophunzira ake.