Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Marko 2:11 - Buku Lopatulika

Ndikuuza iwe, Nyamuka, senza mphasa yako, numuke kwanu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndikuuza iwe, Nyamuka, senza mphasa yako, numuke kwanu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

“Iwe, dzuka, tenga machira ako, uzipita kumudzi.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

“Ndikuwuza iwe, imirira, tenga mphasa yako ndipo pita kwanu.”

Onani mutuwo



Marko 2:11
5 Mawu Ofanana  

Ndipo Yesu anagwidwa chifundo, natansa dzanja namkhudza iye, nanena naye, Ndifuna; khala wokonzedwa.


Koma kuti mudziwe kuti Mwana wa Munthu ali mwini ulamuliro wakukhululukira machimo padziko lapansi (ananena ndi wodwala manjenje),


Ndipo ananyamuka iye pomwepo, nasenza mphasa, natuluka pamaso pa iwo onse; kotero kuti anadabwa onse, nalemekeza Mulungu, nanena kuti, Zotere sitinazione ndi kale lonse.


Wopatsa moyo ndi mzimu; thupi silithandiza konse. Mau amene ndalankhula ndi inu ndiwo mzimu, ndi moyo.