Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Marko 15:9 - Buku Lopatulika

Ndipo Pilato anawayankha, nanena nao, Kodi mufuna kuti ndikumasulireni mfumu ya Ayuda?

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Pilato anawayankha, nanena nao, Kodi mufuna kuti ndikumasulireni mfumu ya Ayuda?

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pilato adaŵafunsa kuti, “Kodi mukufuna kuti ndikumasulireni Mfumu ya Ayudayi?”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

“Kodi mukufuna kuti ndikumasulireni mfumu ya Ayuda?” Pilato anafunsa,

Onani mutuwo



Marko 15:9
7 Mawu Ofanana  

Pakuti anazindikira kuti ansembe aakulu anampereka Iye mwanjiru.


Ndipo khamu la anthu anabwera nayamba kupempha kuti achite monga anali kuwachitira nthawi zonse.


Koma muli nao makhalidwe, akuti ndimamasulira inu mmodzi pa Paska; kodi mufuna tsono kuti ndimasulire inu mfumu ya Ayuda?