Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Marko 15:7 - Buku Lopatulika

Ndipo analipo wina dzina lake Barabasi, womangidwa pamodzi ndi opanduka, amene anapha munthu mumpanduko.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo analipo wina dzina lake Barabasi, wamangidwa pamodzi ndi opanduka, amene anapha munthu mumphandumo.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Panali munthu wina, dzina lake Barabasi, amene anali m'ndende pamodzi ndi anthu ena chifukwa choukira Boma ndi kupha anthu.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Munthu wotchedwa Baraba anali mʼndende pamodzi ndi anthu owukira amene anapha anthu pa nthawi ya chipolowe.

Onani mutuwo



Marko 15:7
5 Mawu Ofanana  

Ndipo pa nthawi yomweyo anali ndi wandende wodziwika, dzina lake Barabasi.


Ndipo ankawamasulira pachikondwerero wandende mmodzi, amene iwo anampempha.


Ndipo khamu la anthu anabwera nayamba kupempha kuti achite monga anali kuwachitira nthawi zonse.


Ndipo anawamasulira amene adaponyedwa m'ndende chifukwa cha mpanduko ndi kupha munthu, amene iwo anampempha; koma anapereka Yesu mwa chifuniro chao.