Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Marko 15:13 - Buku Lopatulika

Ndipo anafuulanso, Mpachikeni pamtanda.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo anafuulanso, Mpachikeni pamtanda.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Anthuwo adafuula kuti, “Mpachikeni pa mtanda!”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Anafuwula kuti, “Mpachikeni!”

Onani mutuwo



Marko 15:13
4 Mawu Ofanana  

Ndipo Pilato anawayankhanso, nati kwa iwo, Pamenepo ndidzachita chiyani ndi Iye amene mumtchula mfumu ya Ayuda?


Ndipo Pilato ananena nao, Pakuti Iye anachita choipa chotani? Koma iwo anafuulitsatu, Mpachikeni Iye.


koma iwo anafuula, nanena, Mpachikeni, mpachikeni pamtanda.


Ndipo ngakhale sanapeze chifukwa cha kumphera, anapempha Pilato kuti aphedwe.