Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Marko 15:11 - Buku Lopatulika

Koma ansembe aakulu anasonkhezera khamulo, kuti makamaka awamasulire Barabasi.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Koma ansembe aakulu anasonkhezera khamulo, kuti makamaka awamasulire Barabasi.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Koma akulu a ansembewo adasonkhezera anthu onse aja kuti apemphe kuŵamasulira Barabasi.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Koma akulu a ansembe anasonkhezera anthu kuti Pilato amasule Baraba mʼmalo mwa Yesu.

Onani mutuwo



Marko 15:11
6 Mawu Ofanana  

Imvani ichi, ansembe inu; mverani, inu nyumba ya Israele; tcherani khutu, inu nyumba ya mfumu; pakuti chiweruzochi chinena inu; pakuti munakhala msampha ku Mizipa, ndi ukonde woyalidwa pa Tabori.


Koma ansembe aakulu ndi akulu anapangira anthu kuti apemphe Barabasi, koma kuti aononge Yesu.


Pakuti anazindikira kuti ansembe aakulu anampereka Iye mwanjiru.


Ndipo Pilato anawayankhanso, nati kwa iwo, Pamenepo ndidzachita chiyani ndi Iye amene mumtchula mfumu ya Ayuda?


Pomwepo anafuulanso, nanena, Si uyu, koma Barabasi. Koma Barabasi anali wachifwamba.


Koma inu munakaniza Woyera ndi Wolungamayo, ndipo munapempha kuti munthu wambanda apatsidwe kwa inu,