Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Marko 14:71 - Buku Lopatulika

Koma iye anayamba kutemberera, ndi kulumbira, Sindimdziwa munthuyu mulikunena.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Koma iye anayamba kutemberera, ndi kulumbira, Sindimdziwa munthuyu mulikunena.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Koma Petro adayamba kudzitemberera nkumalumbira kuti, “Mtheradi, munthu amene mukunenayu ine sindimdziŵa.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Iye anayamba kudzitemberera, nalumbira kuti, “Sindimudziwa munthu ameneyu.”

Onani mutuwo



Marko 14:71
6 Mawu Ofanana  

Masiku ao Yehova anayamba kusadza Israele; ndipo Hazaele anawakantha m'malire onse a Israele,


Mtima ndiwo wonyenga koposa, ndi wosachiritsika, ndani angathe kuudziwa?


Koma anakananso. Ndipo patapita kamphindi, akuimirirapo ananenanso ndi Petro, Zedi uli wa awo; pakutinso uli Mgalileya.


Ndipo pomwepo tambala analira kachiwiri. Ndipo Petro anakumbukira umo Yesu anati kwa iye, kuti, Tambala asanalire kawiri udzandikana katatu. Ndipo pakuganizira ichi analira misozi.


Chifukwa chake iye wakuyesa kuti ali chilili, ayang'anire kuti angagwe.