Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Marko 13:18 - Buku Lopatulika

Ndipo pempherani kuti kusakhale m'nyengo yachisanu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo pempherani kuti kusakhale m'nyengo yachisanu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pempherani kuti zimenezi zisadzaoneke pa nyengo yachisanu,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pempherani kuti zimenezi zisadzachitike nthawi yozizira,

Onani mutuwo



Marko 13:18
2 Mawu Ofanana  

Koma tsoka iwo akukhala ndi pakati, ndi akuyamwitsa ana masiku awo!


Pakuti masiku aja padzakhala chisautso, chonga sichinakhala chinzake kuyambira chiyambi cha chilengedwe chimene Mulungu anachilenga ndi kufikira tsopano, ndipo sichidzakhalanso, nthawi zonse.