Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Marko 13:16 - Buku Lopatulika

ndi iye amene ali kumunda asabwere kudzatenga malaya ake.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

ndi iye amene ali kumunda asabwere kudzatenga malaya ake.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Yemwe ali ku munda, asabwererenso ku nyumba kuti akatenge mwinjiro.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Aliyense amene ali ku munda asabwerere kukatenga mkanjo wake.

Onani mutuwo



Marko 13:16
2 Mawu Ofanana  

ndi iye amene ali pamwamba pa tsindwi asatsike, kapena asalowe kukatulutsa kanthu m'nyumba mwake;


Koma tsoka iwo akukhala ndi pakati, ndi akuyamwitsa ana masiku awo!