Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Marko 12:8 - Buku Lopatulika

Ndipo anamtenga, namupha iye, namtaya kunja kwa munda.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo anamtenga, namupha iye, namtaya kunja kwa munda.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tsono adamugwiradi, namupha nkumuponya kunja kwa mundawo.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndipo anamutenga ndi kumupha, ndipo anamuponya kunja kwa munda wamphesa.

Onani mutuwo



Marko 12:8
6 Mawu Ofanana  

Mverani fanizo lina: Panali munthu, mwini banja, amene analima munda wampesa, nauzunguniza linga, nakumba umo moponderamo mphesa, namanga nsanja, naukongoletsa kwa olima munda, namuka kwina.


Ndipo anamtenga iye, namponya kunja kwa munda, namupha.


Koma olima ajawo, ananena mwa iwo okha, Ameneyu ndiye wolowa nyumba; tiyeni timuphe iye, ndipo mundawu udzakhala wathu.


Pamenepo mwini munda adzachita chiyani? Adzafika, nadzaononga olimawo, nadzapereka mundawo kwa ena.


Ndipo anamponya kunja kwa mundawo, namupha. Pamenepo mwini munda wampesawo adzawachitira chiyani?