Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Marko 12:4 - Buku Lopatulika

Ndipo anatumanso kapolo wina kwa iwo; ndipo ameneyu anamlasa mutu, namchitira zomchititsa manyazi.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo anatumanso kapolo wina kwa iwo; ndipo ameneyu anamlasa mutu, namchitira zomchititsa manyazi.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Munthu uja adatumanso wantchito wina, koma alimi aja adamtema m'mutu nkumunyazitsa.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Kenaka anatumizanso wantchito wina kwa iwo. Iwo anamumenya munthuyo pamutu ndipo anamuzunza mochititsa manyazi.

Onani mutuwo



Marko 12:4
5 Mawu Ofanana  

Ndipo Hanuni anatenga anyamata a Davide, nawameta, nadula malaya ao pakati kufikira m'matako, nawaleka achoke.


Indedi Mulungu adzaphwanya mutu wa adani ake, pakati pamutu pa iye woyendabe m'kutsutsika kwake.


Ndipo iwo anamtenga iye, nampanda, namchotsa wopanda kanthu.


Ndipo anatuma wina; iyeyu anamupha; ndi ena ambiri; ena anawapanda, ndi ena anawapha.


Ndipo anatumizanso kapolo wina; ndipo iyenso anampanda, namchitira chipongwe, nambweza, wopanda kanthu.