Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Marko 11:6 - Buku Lopatulika

Ndipo anati kwa iwo monga momwe ananena Yesu: ndipo anawalola iwo apite naye.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo anati kwa iwo monga momwe ananena Yesu: ndipo anawalola iwo apite naye.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ophunzirawo adaŵayankha monga momwe adaaŵauzira Yesu. Tsono anthuwo adaŵalola kuti ammasule.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Iwo anayankha monga mmene Yesu anawawuzira, ndipo anthu aja anawalola kuti apite.

Onani mutuwo



Marko 11:6
2 Mawu Ofanana  

Ndipo ena akuima kumeneko ananena nao, Muchita chiyani ndi kumasula mwana wa bulu?


Ndipo anabwera naye mwana wa bulu kwa Yesu, naika zovala zao pa iye, ndipo Iye anakhala pamenepo.