Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Marko 11:5 - Buku Lopatulika

Ndipo ena akuima kumeneko ananena nao, Muchita chiyani ndi kumasula mwana wa bulu?

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo ena akuima kumeneko ananena nao, Muchita chiyani ndi kumasula mwana wa bulu?

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Anthu amene adaali pamenepo adaŵafunsa kuti, “Inu nchiyani chimenecho, buluyo mukummasuliranji?”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

anthu ena amene anayima pomwepo anafunsa kuti, “Mukuchita chiyani, kumasula mwana wabuluyo?”

Onani mutuwo



Marko 11:5
3 Mawu Ofanana  

nanena kwa iwo, Mukani kumudzi wopenyana ndi inu, ndipo pomwepo mudzapeza bulu womangidwa, ndi mwana wake pamodzi naye, masulani iwo, mudze nao kwa Ine.


Ndipo anachoka, napeza mwana wa bulu womangidwa pakhomo, pabwalo m'khwalala, nammasula iye.


Ndipo anati kwa iwo monga momwe ananena Yesu: ndipo anawalola iwo apite naye.