Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Marko 11:12 - Buku Lopatulika

Ndipo m'mawa mwake, atatuluka ku Betaniya, Iye anamva njala.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo m'mawa mwake, atatuluka ku Betaniya, Iye anamva njala.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

M'maŵa mwake, pamene iwo ankachoka ku Betaniya kuja, Yesu adaamva njala.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Mmawa mwake pamene amachoka ku Betaniya, Yesu anamva njala.

Onani mutuwo



Marko 11:12
9 Mawu Ofanana  

Ndipo pamene Iye analibe kudya masiku makumi anai usana ndi usiku, pambuyo pake anamva njala.


Ndipo anaona mkuyu kutali, uli ndi masamba; ndipo anadza Iye, kuti kapena akapezapo kanthu: ndipo m'mene anafikako anapeza palibe kanthu koma masamba okha; pakuti siinali nyengo yake ya nkhuyu.


Ndipo m'mene anapitapo m'mawa mwake, anaona kuti mkuyu uja unafota, kuyambira kumizu.


kukayesedwa ndi mdierekezi masiku makumi anai. Ndipo Iye sanadye kanthu masiku awo; ndipo pamene anatha anamva njala.


Chitapita ichi Yesu, podziwa kuti zonse zidatha pomwepo kuti lembo likwaniridwe, ananena, Ndimva ludzu.


Potero kudamuyenera kufanizidwa ndi abale m'zonse, kuti akadzakhala mkulu wa ansembe wachifundo ndi wokhulupirika m'zinthu za kwa Mulungu, kuti apereke dipo la zoipa za anthu.