Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Marko 10:9 - Buku Lopatulika

Chifukwa chake chimene Mulungu anachimanga pamodzi, asachilekanitse munthu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Chifukwa chake chimene Mulungu anachimanga pamodzi, asachilekanitse munthu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tsono zimene Mulungu wazilumikiza pamodzi, munthu asazilekanitse.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Chifukwa chake chimene Mulungu wachilumikiza pamodzi, munthu wina asachilekanitse.”

Onani mutuwo



Marko 10:9
4 Mawu Ofanana  

Ndipo m'nyumba ophunzira anamfunsanso za chinthu ichi.


ndipo awiriwa adzakhala thupi limodzi: kotero kuti salinso awiri, koma thupi limodzi.