Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Marko 10:8 - Buku Lopatulika

ndipo awiriwa adzakhala thupi limodzi: kotero kuti salinso awiri, koma thupi limodzi.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

ndipo awiriwa adzakhala thupi limodzi: kotero kuti salinso awiri, koma thupi limodzi.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

ndipo aŵiriwo adzasanduka thupi limodzi. Choncho tsopano salinso aŵiri, koma thupi limodzi.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

ndipo awiriwo adzakhala thupi limodzi.’ Potero sali awirinso, koma mmodzi.

Onani mutuwo



Marko 10:8
4 Mawu Ofanana  

Chifukwa chotero mwamuna adzasiya atate wake ndi amake nadzadziphatika kwa mkazi wake: ndipo adzakhala thupi limodzi.


Chifukwa chake chimene Mulungu anachimanga pamodzi, asachilekanitse munthu.


Kapena simudziwa kuti iye wophatikidwa ndi mkazi wachiwerewere ali thupi limodzi? Pakuti awiriwo, ati, adzakhala thupi limodzi.


Koteronso amuna azikonda akazi ao a iwo okha monga ngati matupi a iwo okha. Wokonda mkazi wa iye yekha, adzikonda yekha;