Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Marko 10:7 - Buku Lopatulika

Chifukwa chake mwamuna adzasiya atate wake ndi amai wake, ndipo adzaphatikizana ndi mkazi wake;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Chifukwa chake mwamuna adzasiya atate wake ndi amai wake, ndipo adzaphatikizana ndi mkazi wake;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Nchifukwa chake mwamuna azisiya atate ndi amai, nakaphatikizana ndi mkazi wake,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

‘Pa chifukwa ichi mwamuna adzasiya abambo ake ndi amayi ake nakaphatikana ndi mkazi wake,

Onani mutuwo



Marko 10:7
3 Mawu Ofanana  

Chifukwa chotero mwamuna adzasiya atate wake ndi amake nadzadziphatika kwa mkazi wake: ndipo adzakhala thupi limodzi.


Chifukwa cha ichi munthu azisiya atate ndi amai, nadzaphatikizana ndi mkazi wake; ndipo iwo awiri adzakhala thupi limodzi.