Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Marko 10:44 - Buku Lopatulika

ndipo aliyense amene afuna kukhala woyamba mwa inu adzakhala kapolo wa onse.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

ndipo amene aliyense afuna kukhala woyamba mwa inu adzakhala kapolo wa onse.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ndipo aliyense wofuna kukhala mtsogoleri pakati panu, azikhala kapolo wa onse.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

ndipo aliyense amene akufuna kukhala wamkulu akhale kapolo wa onse.

Onani mutuwo



Marko 10:44
5 Mawu Ofanana  

Ndipo kwa iye wofuna kupita nawe kumlandu ndi kutenga malaya ako, umlolezenso chofunda chako.


Koma mwa inu sikutero ai; koma aliyense amene afuna kukhala wamkulu mwa inu adzakhala mtumiki wanu;


Pakuti ndithu, Mwana wa Munthu sanadze kutumikiridwa, koma kutumikira, ndi kupereka moyo wake dipo la kwa anthu ambiri.


Ndipo m'mene anakhala pansi anaitana khumi ndi awiriwo; nanena nao, Ngati munthu afuna kukhala woyamba, akhale wakuthungo wa onse, ndi mtumiki wa onse.


koma anadzikhuthula yekha, natenga maonekedwe a kapolo, nakhala m'mafanizidwe a anthu;