Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Marko 10:16 - Buku Lopatulika

Ndipo Iye anatiyangata, natidalitsa, ndi kuika manja ake pa ito.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Iye anatiyangata, natidalitsa, ndi kuika manja ake pa ito.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Atatero adayamba kuŵafungata anawo, naŵasanjika manja ndi kuŵadalitsa.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndipo ananyamula ana mʼmanja ake, ndi kuyika manja ake pa iwo nawadalitsa.

Onani mutuwo



Marko 10:16
8 Mawu Ofanana  

Iye adzadyetsa zoweta zake ngati mbusa, nadzasonkhanitsa anaankhosa m'manja mwake, nadzawatengera pa chifuwa chake, ndipo adzatsogolera bwinobwino zimene ziyamwitsa.


Ndipo pamene iwo analikudya, Iye anatenga mkate, ndipo pamene anadalitsa, ananyema, napereka kwa iwo, kuti, Tengani; thupi langa ndi ili.


Ndipo anatenga kamwana, nakaika pakati pao, nakayangata, nanena nao,


Mudzakhala odala m'mzinda, ndi odala kubwalo.