Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Marko 10:10 - Buku Lopatulika

Ndipo m'nyumba ophunzira anamfunsanso za chinthu ichi.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo m'nyumba ophunzira anamfunsanso za chinthu ichi.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pamene adaloŵanso m'nyumba, ophunzira adamufunsanso Yesu za nkhani yomweyi.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pamene analinso mʼnyumba, ophunzira anamufunsa Yesu za izi.

Onani mutuwo



Marko 10:10
5 Mawu Ofanana  

Ndipo Iye ananena nao, Munthu aliyense akachotsa mkazi wake, nakakwatira wina, achita chigololo kulakwira mkaziyo;


Chifukwa chake chimene Mulungu anachimanga pamodzi, asachilekanitse munthu.


Ndipo pamene anakhala pa yekha, iwo amene anali pafupi ndi Iye pamodzi ndi khumi ndi awiriwo anamfunsa za mafanizo.


Ndipo pamene Iye adalowa m'nyumba, ophunzira ake anamfunsa m'tseri, kuti, Nanga bwanji sitinathe ife kuutulutsa?


Ndipo iwo anadza ku Kapernao; ndipo pamene anakhala m'nyumba, Iye anawafunsa, Munalikutsutsana ninji panjira?