Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Marko 1:43 - Buku Lopatulika

Ndipo anamuuzitsa, namtulutsa pomwepo,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo anamuuzitsa, namtulutsa pomwepo,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tsono Yesu adamlamula kuti apite, namuuza mau amphamvu.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Nthawi yomweyo Yesu anamuwuza kuti apite koma anamuchenjeza kuti,

Onani mutuwo



Marko 1:43
7 Mawu Ofanana  

Ndipo maso ao anaphenyuka. Ndipo Yesu anawauzitsa iwo, nanena, Yang'anirani, asadziwe munthu aliyense.


Ndipo pomwepo khate linamchoka, ndipo anakonzedwa.


nanena naye, Ona, usati unene kanthu kwa munthu aliyense: koma muka, ukadzionetse kwa wansembe, nupereke pa makonzedwe ako zimene adalamulira Mose, zikhale mboni kwa iwo.


Ndipo anailimbitsira mau kuti isamuulule Iye.


Ndipo anawalamulira kwambiri kuti asadziwe ichi munthu mmodzi, nawauza kuti ampatse iye kudya.


Ndipo anawalamulira kuti asauze munthu aliyense; koma monga momwe Iye anawalamulitsa momwenso makamaka analalikira kopambana.


Ndipo atate wake ndi amake anadabwa; ndipo analamulira iwo asauze munthu aliyense chimene chinachitika.