Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Marko 1:18 - Buku Lopatulika

Ndipo pomwepo anasiya makoka ao, namtsata Iye.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo pomwepo anasiya makoka ao, namtsata Iye.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pomwepo iwo adasiya makoka ao, namamtsatadi.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Nthawi yomweyo anasiya makoka awo namutsata Iye.

Onani mutuwo



Marko 1:18
9 Mawu Ofanana  

Ndipo iwo anasiya pomwepo makokawo, namtsata Iye.


Ndipo Yesu ananena nao, Idzani pambuyo panga, ndipo ndidzakusandutsani inu asodzi a anthu.


Ndipo atapita patsogolo pang'ono, anaona Yakobo, mwana wa Zebedeo, ndi Yohane mbale wake, iwonso anali m'chombo nakonza makoka ao.


Chifukwa chake tsono, yense wa inu amene sakaniza zonse ali nazo, sangathe kukhala wophunzira wanga.


Ndipo m'mene iwo anakocheza ngalawa zao pamtunda, anasiya zonse, namtsata Iye.


Komatu zenizeninso ndiyesa zonse zikhale chitayiko chifukwa cha mapambanidwe a chizindikiritso cha Khristu Yesu Ambuye wanga, chifukwa cha Iyeyu ndinatayikitsa zinthu zonse, ndipo ndiziyesa zapadzala, kuti ndikadzionjezere Khristu,