Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Maliro 3:2 - Buku Lopatulika

Wanditsogolera, nandiyendetsa mumdima, si m'kuunika ai.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Wanditsogolera, nandiyendetsa mumdima, si m'kuunika ai.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Adandiyendetsa ndi kubwera nane mu mdima mopanda nkuŵala komwe.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Wandipititsa kutali ndipo wandiyendetsa mu mdima osati mʼkuwala;

Onani mutuwo



Maliro 3:2
11 Mawu Ofanana  

Adzamkankha achoke kukuunika alowe kumdima; adzampirikitsa achoke m'dziko lokhalamo anthu.


Muja ndinayembekeza chokoma chinadza choipa, ndipo polindira kuunika unadza mdima.


Chifukwa chake chiweruziro chili patali ndi ife, ndi chilungamo sichitipeza; tiyang'anira kuunika, koma taona mdima; tiyang'anira kuyera, koma tiyenda mu usiku.


Lemekezani Yehova Mulungu wanu, kusanade, mapazi anu asanaphunthwe pa mapiri achizirezire; nimusanayembekeze kuunika, Iye asanasandutse kuunikaku mthunzi wa imfa, ndi kukuyesa mdima wa bii.


Ndinaona dziko lapansi, ndipo taona, linali lopasuka lopanda kanthu; ndipo ndinaona kumwamba, kunalibe kuunika.


Ambuye waphimbatu ndi mtambo mwana wamkazi wa Ziyoni, pomkwiyira! Wagwetsa pansi kuchokera kumwamba kukoma kwake kwa Israele; osakumbukira poponda mapazi ake tsiku la mkwiyo wake.


ndipo mudzafufuza usana, monga wakhungu amafufuza mumdima, ndipo simudzapindula nazo njira zanu; koma mudzakhala wopsinjika, nadzakuberani masiku onse, wopanda wina wakukupulumutsani.


mafunde oopsa a nyanja, akuwinduka thovu la manyazi a iwo okha; nyenyezi zosokera, zimene mdima wakuda bii udazisungikira kosatha.


Angelonso amene sanasunge chikhalidwe chao choyamba, komatu anasiya pokhala paopao, adawasunga m'ndende zosatha pansi pa mdima, kufikira chiweruziro cha tsiku lalikulu.