Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Malaki 3:9 - Buku Lopatulika

Mutembereredwa ndi temberero; pakuti mundilanda Ine, ndinu mtundu uwu wonse.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Mutembereredwa ndi temberero; pakuti mundilanda Ine, ndinu mtundu uwu wonse.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ndinu otembereredwa nonsenu, mtundu wanu wonse, chifukwa choti mumandibera.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Mtundu wanu wonse ndinu otembereredwa, chifukwa mukundibera.

Onani mutuwo



Malaki 3:9
8 Mawu Ofanana  

Chifukwa chake ndidzaipitsa akulu a Kachisi, ndipo ndidzasanduliza Yakobo akhale temberero, ndi Israele akhale chitonzo.


Ndipo anati kwa ine, Ili ndi temberero lilikutulukira padziko lonse; pakuti aliyense wakuba adzapirikitsidwa kuno monga mwa ili; ndi aliyense wakulumbira zonama adzapirikitsidwa kuno monga mwa ili.


Mukapanda kumvera, mukapanda kuliika mumtima mwanu, kupatsa dzina langa ulemerero, ati Yehova wa makamu, ndidzakutumizirani temberero, ndi kutemberera madalitso anu; inde, ndawatemberera kale chifukwa simuliika mumtima.


Kodi Akani mwana wa Zera sanalakwe m'choperekedwacho, ndipo mkwiyo unagwera gulu lonse la Israele? Osangoonongeka yekha munthuyo mu mphulupulu yake.