Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Machitidwe a Atumwi 9:7 - Buku Lopatulika

Ndipo amunawo akumperekeza iye anaima duu, atamvadi mau, koma osaona munthu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo amunawo akumperekeza iye anaima duu, atamvadi mau, koma osaona munthu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Anthu amene anali naye pa ulendowo adaima, atangoti chete. Mauwo ankaŵamva, koma osaona munthu.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Anthu amene anali naye paulendo, anasowa chonena; iwo anamva mawu koma sanaone wina aliyense.

Onani mutuwo



Machitidwe a Atumwi 9:7
5 Mawu Ofanana  

Ndipo ine Daniele ndekha ndinaona masomphenyawo; pakuti anthu anali nane sanaone masomphenyawo; koma kunawagwera kunjenjemera kwakukulu, nathawa kubisala.


Chifukwa chake khamu la anthu akuimirirako, ndi kuwamva ananena kuti kwagunda. Ena ananena, Mngelo walankhula ndi Iye.


Ndipo iwo akukhala nane anaonadi kuunika, koma sanamve mau akulankhula nane.