Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Machitidwe a Atumwi 7:57 - Buku Lopatulika

Koma anafuula ndi mau aakulu, natseka m'makutu mwao, namgumukira iye ndi mtima umodzi;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Koma anafuula ndi mau akulu, natseka m'makutu mwao, namgumukira iye ndi mtima umodzi;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Koma iwo adafuula kwambiri, natseka m'makutu mwao, namgudukira onse pamodzi.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Koma iwo anatseka mʼmakutu mwawo, ndipo anafuwula kolimba, onse anathamangira kwa iye,

Onani mutuwo



Machitidwe a Atumwi 7:57
8 Mawu Ofanana  

Ululu wao ukunga wa njoka; akunga mphiri yogontha m'khutu, itseka m'khutu mwake.


Wotseka makutu ake polira waumphawi, nayenso adzalira koma osamvedwa.


Koma anakana kumvera, nakaniza phewa lao, natseka makutu ao, kuti asamve.


Munthu uyu anagwiridwa ndi Ayuda, ndipo akadaphedwa ndi iwo; pamenepo ndinafikako ine ndi asilikali, ndipo ndinamlanditsa pakumva kuti ndiye Mroma.


Koma pakumva izi analaswa mtima, namkukutira mano.


nati, Taonani, ndipenya mu Mwamba motseguka, ndi Mwana wa Munthu alikuimirira padzanja lamanja la Mulungu.


ndipo anamtaya kunja kwa mzinda, namponya miyala; ndipo mbonizo zinaika zovala zao pa mapazi a mnyamata dzina lake Saulo.