Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Machitidwe a Atumwi 7:21 - Buku Lopatulika

ndipo pakutayika iye, anamtola mwana wamkazi wa Farao, namlera akhale mwana wake.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

ndipo pakutayika iye, anamtola mwana wamkazi wa Farao, namlera akhale mwana wake.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

koma atamsiya pamtsinje paja, mwana wamkazi wa Farao adamtola, namlera ngati mwana wake.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Atakamutaya, mwana wamkazi wa Farao anamutola nakamulera ngati mwana wake.

Onani mutuwo



Machitidwe a Atumwi 7:21
3 Mawu Ofanana  

Ndinati, Ndikadawauzira ndithu, ndikadafafaniza chikumbukiro chao mwa anthu.


Ndi chikhulupiriro Mose, atakula msinkhu, anakana kutchedwa mwana wake wa mwana wamkazi wa Farao;