Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Machitidwe a Atumwi 7:18 - Buku Lopatulika

kufikira inauka mfumu ina pa Ejipito, imene siinamdziwe Yosefe.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

kufikira inauka mfumu ina pa Ejipito, imene siinamdziwa Yosefe.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pambuyo pake mfumu ina imene sidadziŵe Yosefe, idayamba kulamulira ku Ejipito.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pambuyo pake mfumu yatsopano imene sinkamudziwa Yosefe, inayamba kulamulira dziko la Igupto.

Onani mutuwo



Machitidwe a Atumwi 7:18
2 Mawu Ofanana  

Pamenepo inalowa mfumu yatsopano mu ufumu wa Ejipito, imene siinadziwe Yosefe.


Imeneyo inachenjerera fuko lathu, niwachitira choipa makolo athu, niwatayitsa tiana tao, kuti tingakhale ndi moyo.