Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Machitidwe a Atumwi 7:1 - Buku Lopatulika

Ndipo mkulu wa ansembe anati, Zitero izi kodi?

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo mkulu wa ansembe anati, Zitero izi kodi?

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Mkulu wa ansembe onse adafunsa Stefano kuti, “Kodi zimenezi nzoona?”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Kenaka mkulu wa ansembe anafunsa Stefano kuti, “Kodi zimene akukunenerazi ndi zoona?”

Onani mutuwo



Machitidwe a Atumwi 7:1
7 Mawu Ofanana  

Ndipo anampenyetsetsa onse akukhala m'bwalo la akulu a milandu, naona nkhope yake ngati nkhope ya mngelo.


Ndipo Stefano anati, Amuna inu, abale, ndi atate, tamverani. Mulungu wa ulemerero anaonekera kwa kholo lathu Abrahamu, pokhala iye mu Mesopotamiya, asanayambe kukhala mu Harani;