Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Machitidwe a Atumwi 5:7 - Buku Lopatulika

Koma atapita monga maora atatu, ndipo mkazi wake, wosadziwa chidachitikacho, analowa.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Koma atapita monga maora atatu, ndipo mkazi wake, wosadziwa chidachitikacho, analowa.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Patapita ngati maora atatu, mkazi wake adaloŵa, osadziŵa zimene zachitika.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Patapita maora atatu mkazi wake analowa, wosadziwa zimene zinachitika.

Onani mutuwo



Machitidwe a Atumwi 5:7
2 Mawu Ofanana  

Ndipo ananyamuka anyamata, namkulunga, namnyamula, natuluka naye, namuika.


Ndipo Petro ananena naye, Undiuze, ngati munagulitsa mundawo pa mtengo wakuti. Ndipo ananena, Inde, wakuti.