Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Machitidwe a Atumwi 5:6 - Buku Lopatulika

Ndipo ananyamuka anyamata, namkulunga, namnyamula, natuluka naye, namuika.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo ananyamuka anyamata, namkulunga, namnyamula, natuluka naye, namuika.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tsono achinyamata adabwera namkulunga m'nsalu. Adamnyamula nakamuika m'manda.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Kenaka anyamata anafika, nakulunga thupi lake, ndipo anamunyamula ndi kukamuyika mʼmanda.

Onani mutuwo



Machitidwe a Atumwi 5:6
5 Mawu Ofanana  

Ndipo anatenga Abisalomu namponya m'chidzenje chachikulu kunkhalangoko; naunjika pamwamba pake mulu waukulu ndithu wamiyala; ndipo Aisraele onse anathawa yense ku hema wake.


Pamenepo anatenga mtembo wa Yesu, nauzenenga ndi nsalu zabafuta pamodzi ndi zonunkhira, monga mwa maikidwe a maliro a Ayuda.


Koma atapita monga maora atatu, ndipo mkazi wake, wosadziwa chidachitikacho, analowa.


mtembo wake usakhale pamtengo usiku wonse, koma mumuike ndithu tsiku lomwelo; pakuti wopachikidwa pamtengo atembereredwa ndi Mulungu; kuti mungadetse dziko lanu limene Yehova Mulungu wanu akupatsani likhale cholowa chanu.