Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Machitidwe a Atumwi 3:9 - Buku Lopatulika

Ndipo anthu onse anamuona iye, alikuyenda ndi kuyamika Mulungu;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo anthu onse anamuona iye, alikuyenda ndi kuyamika Mulungu;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Anthu onse adamuwona akuyenda ndi kutamanda Mulungu.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Anthu onse atamuona akuyenda ndiponso kuyamika Mulungu,

Onani mutuwo



Machitidwe a Atumwi 3:9
5 Mawu Ofanana  

Ndipo pamene Iye anatero, onse aja akutsutsana naye ananyazitsidwa; ndipo anthu onse a m'khamu anakondwera ndi zinthu zonse za ulemererozo zinachitidwa ndi Iye.


Pamene makamu anaona chimene anachita Paulo, anakweza mau ao, nati m'chinenero cha Likaoniya, Milungu yatsikira kwa ife monga anthu.


kuti, Tidzawachitira chiyani anthu awa? Pakutitu chaoneka kwa onse akukhala mu Yerusalemu kuti chizindikiro chozindikirika chachitidwa ndi iwo, ndipo sitingathe kukana.


Koma m'mene anawaopsanso anawamasula, osapeza kanthu kakuwalanga, chifukwa cha anthu; pakuti onse analemekeza Mulungu chifukwa cha chomwe chidachitika.