Ndipo pamene Iye anatero, onse aja akutsutsana naye ananyazitsidwa; ndipo anthu onse a m'khamu anakondwera ndi zinthu zonse za ulemererozo zinachitidwa ndi Iye.
Machitidwe a Atumwi 3:9 - Buku Lopatulika Ndipo anthu onse anamuona iye, alikuyenda ndi kuyamika Mulungu; Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014 Ndipo anthu onse anamuona iye, alikuyenda ndi kuyamika Mulungu; Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa Anthu onse adamuwona akuyenda ndi kutamanda Mulungu. Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero Anthu onse atamuona akuyenda ndiponso kuyamika Mulungu, |
Ndipo pamene Iye anatero, onse aja akutsutsana naye ananyazitsidwa; ndipo anthu onse a m'khamu anakondwera ndi zinthu zonse za ulemererozo zinachitidwa ndi Iye.
Pamene makamu anaona chimene anachita Paulo, anakweza mau ao, nati m'chinenero cha Likaoniya, Milungu yatsikira kwa ife monga anthu.
kuti, Tidzawachitira chiyani anthu awa? Pakutitu chaoneka kwa onse akukhala mu Yerusalemu kuti chizindikiro chozindikirika chachitidwa ndi iwo, ndipo sitingathe kukana.
Koma m'mene anawaopsanso anawamasula, osapeza kanthu kakuwalanga, chifukwa cha anthu; pakuti onse analemekeza Mulungu chifukwa cha chomwe chidachitika.