Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Machitidwe a Atumwi 3:5 - Buku Lopatulika

Ndipo iye anavomereza iwo, nalingirira kuti adzalandira kanthu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo iye anavomereza iwo, nalingirira kuti adzalandira kanthu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Iye nkuŵayang'anadi namaganiza kuti alandira kanthu kwa iwo.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Munthuyo anawayangʼanitsitsa kuyembekezera kuti alandira kanthu kuchokera kwa iwo.

Onani mutuwo



Machitidwe a Atumwi 3:5
2 Mawu Ofanana  

Ndipo Petro, pompenyetsetsa iye pamodzi ndi Yohane, anati, Tiyang'ane ife.


Koma Petro anati, Siliva ndi golide ndilibe; koma chimene ndili nacho, ichi ndikupatsa, M'dzina la Yesu Khristu Mnazarayo, yenda.