Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Machitidwe a Atumwi 24:4 - Buku Lopatulika

Koma kuti ndingaonjeze kukulemetsani ndikupemphani mutimvere mwachidule ndi chifatso chanu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Koma kuti ndingaonjeze kukulemetsani ndikupemphani mutimvere mwachidule ndi chifatso chanu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pepani sindikufuna kukutayitsani nthaŵi, komabe ndimapempha kuti mundikomere mtima, mungomvapo mau athuŵa mwachidule.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Koma kuti tisakuchedwetseni, ndikupempha kuti mwa kuleza mtima kwanu mutimvere ife.

Onani mutuwo



Machitidwe a Atumwi 24:4
5 Mawu Ofanana  

tizilandira ndi chiyamiko chonse, monsemo ndi ponsepo, Felikisi womveka inu.


Pakuti tapeza munthuyu ali ngati mliri, ndi woutsa mapanduko kwa Ayuda onse m'dziko lonse lokhalamo anthu, ndi mtsogoleri wa mpanduko wa Anazarene;


ndi umo anandizindikiritsa chinsinsicho mwa vumbulutso, monga ndinalemba kale mwachidule,


Kufatsa kwanu kuzindikirike ndi anthu onse. Ambuye ali pafupi.


Ndipo ndinene chiyaninso? Pakuti idzandiperewera nthawi ndifotokozere za Gideoni, Baraki, Samisoni, Yefita; za Davide, ndi Samuele ndi aneneri;