Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Machitidwe a Atumwi 24:3 - Buku Lopatulika

tizilandira ndi chiyamiko chonse, monsemo ndi ponsepo, Felikisi womveka inu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

tizilandira ndi chiyamiko chonse, monsemo ndi ponsepo, Felikisi womveka inu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Zonsezi timazilandira moyamika kwambiri ponseponse mwa njira iliyonse.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Wolemekezeka Felike ife timazilandira zimenezi moyamika kwambiri ponseponse ndi mwa njira iliyonse.

Onani mutuwo



Machitidwe a Atumwi 24:3
7 Mawu Ofanana  

kuyambira pachiyambi, ndinayesa nkokoma inenso, amene ndinalondalonda mosamalitsa zinthu zonse kuyambira pachiyambi, kulembera kwa iwe tsatanetsatane, Teofilo wabwinotu iwe;


ndiponso mukonzeretu nyama zobereka amkwezepo Paulo, nampereke wosungika kwa Felikisi kazembeyo.


Klaudio Lisiasi kwa kazembe womveketsa Felikisi, ndikupatsani moni.


iwowo, m'mene anafika ku Kesareya, anapereka kalata kwa kazembe, naperekanso Paulo kwa iye.


Ndipo pamene adamuitana, Tertulo anayamba kumnenera ndi kunena, Popeza tili nao mtendere wambiri mwa inu, ndipo mwa kuganiziratu kwanu muukonzera mtundu wathu zotiipsa,


Koma kuti ndingaonjeze kukulemetsani ndikupemphani mutimvere mwachidule ndi chifatso chanu.


Koma Paulo anati, Ndilibe misala, Fesito womvekatu; koma nditulutsa mau a choonadi ndi odziletsa.