Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Machitidwe a Atumwi 22:9 - Buku Lopatulika

Ndipo iwo akukhala nane anaonadi kuunika, koma sanamve mau akulankhula nane.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo iwo akukhala nane anaonadi kuunika, koma sanamva mau akulankhula nane.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Anzanga apaulendo adaakuwona kuŵalako, koma mau a amene ankalankhula naneyo sadaŵamve.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Anzanga a paulendo anaona kuwalako, koma sanamve mawuwo, a Iye amene amayankhula nane.

Onani mutuwo



Machitidwe a Atumwi 22:9
4 Mawu Ofanana  

Ndipo ine Daniele ndekha ndinaona masomphenyawo; pakuti anthu anali nane sanaone masomphenyawo; koma kunawagwera kunjenjemera kwakukulu, nathawa kubisala.


dzuwa lamsana, ndinaona panjira, Mfumu, kuunika kochokera kumwamba kowalitsa koposa dzuwa kunawala pondizinga ine ndi iwo akundiperekeza.


Ndipo amunawo akumperekeza iye anaima duu, atamvadi mau, koma osaona munthu.