Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Machitidwe a Atumwi 22:2 - Buku Lopatulika

Ndipo pakumva kuti analankhula nao m'chinenedwe cha Chihebri, anaposa kukhala chete; ndipo anati,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo pakumva kuti analankhula nao m'chinenedwe cha Chihebri, anaposa kukhala chete; ndipo anati:

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pamene iwo adamumva akulankhula nawo pa Chiyuda, adakhala chete kopambana. Tsono Paulo anati,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Atamva iye akuyankhula Chihebri, anakhala chete. Kenaka Paulo anati,

Onani mutuwo



Machitidwe a Atumwi 22:2
2 Mawu Ofanana  

Pamene Iye anali chilankhulire ndi makamu, onani, amake ndi abale ake anaima panja, nafuna kulankhula naye.


Ndipo m'mene adamlola, Paulo anaimirira pamakwerero, natambalitsira anthu dzanja; ndipo pokhala chete onse, analankhula nao m'chinenedwe cha Chihebri, nanena: